Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Aya 75

Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Chewa - Aya 75 Aya count 129

۞ وَمِنْهُم مَّنْ عَٰهَدَ ٱللَّهَ لَئِنْ ءَاتَىٰنَا مِن فَضْلِهِۦ لَنَصَّدَّقَنَّ وَلَنَكُونَنَّ مِنَ ٱلصَّٰلِحِينَ ﴿٧٥﴾
Pakati pawo alipo amene adalonjeza Allah kuti, “Ngati atipatsa zabwino zake (chuma) tidzapereka sadaka ndi kukhala m’gulu la ochita zabwino.”
Share