Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Aya 73

Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Chewa - Aya 73 Aya count 129

يَٰٓأَيُّهَا ٱلنَّبِىُّ جَٰهِدِ ٱلْكُفَّارَ وَٱلْمُنَٰفِقِينَ وَٱغْلُظْ عَلَيْهِمْ ۚ وَمَأْوَىٰهُمْ جَهَنَّمُ ۖ وَبِئْسَ ٱلْمَصِيرُ ﴿٧٣﴾
E iwe Mneneri! Limbana ndi osakhulupirira ndi achiphamaso ndipo uwaumire mtima. Mbuto yawo ndi ku Jahannam. Taonani kuipa kwa malo obwerera.
Share