Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Aya 58

Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Chewa - Aya 58 Aya count 129

وَمِنْهُم مَّن يَلْمِزُكَ فِى ٱلصَّدَقَٰتِ فَإِنْ أُعْطُوا۟ مِنْهَا رَضُوا۟ وَإِن لَّمْ يُعْطَوْا۟ مِنْهَآ إِذَا هُمْ يَسْخَطُونَ ﴿٥٨﴾
Ndipo alipo ena mwa iwo (achiphamaso) amene akukunyogodola mkugawa kwako sadaka. Akapatsidwa kanthu m’menemo amakondwera koma akapanda kupatsidwa akukwiya nawe.
Share