Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Aya 56

Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Chewa - Aya 56 Aya count 129

وَيَحْلِفُونَ بِٱللَّهِ إِنَّهُمْ لَمِنكُمْ وَمَا هُم مِّنكُمْ وَلَٰكِنَّهُمْ قَوْمٌۭ يَفْرَقُونَ ﴿٥٦﴾
Ndipo akulumbira (m’dzina la) Allah kuti iwo ali pamodzi ndi inu; pomwe iwo sali pamodzi nanu koma ndithu iwo ndi anthu amantha.
Share