Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Aya 110

Surah At-Taubah ( The Repentance ) - Chewa - Aya 110 Aya count 129

لَا يَزَالُ بُنْيَٰنُهُمُ ٱلَّذِى بَنَوْا۟ رِيبَةًۭ فِى قُلُوبِهِمْ إِلَّآ أَن تَقَطَّعَ قُلُوبُهُمْ ۗ وَٱللَّهُ عَلِيمٌ حَكِيمٌ ﴿١١٠﴾
Chomanga chawo chomwe adachimanga sichileka kudzetsa chikaiko ndi kusakhazikika m’mitima mwawo kufikira mitima yawo itaduka (ndi madandaulo kapena imfa). Ndipo Allah Ngodziwa (chilichonse), Ngwanzeru zakuya (m’zochitachita Zake).
Share