Surah Al-Fajr ( The Dawn ) - Aya 9

Surah Al-Fajr ( The Dawn ) - Chewa - Aya 9 Aya count 30

وَثَمُودَ ٱلَّذِينَ جَابُوا۟ ٱلصَّخْرَ بِٱلْوَادِ ﴿٩﴾
Ndi Asamudu, (anthu a mneneri Swaleh) amene adali kudula matanthwe ku chigwa (chotchedwa Wadi Qura ndi kumamanga nyumba zikuluzikulu)?
Share