Surah Al-Inshiqaq (The Splitting Asunder) - Aya 10

Surah Al-Inshiqaq (The Splitting Asunder) - Chewa - Aya 10 Aya count 25

وَأَمَّا مَنْ أُوتِىَ كِتَٰبَهُۥ وَرَآءَ ظَهْرِهِۦ ﴿١٠﴾
Koma yemwe adzapatsidwe kaundula wa zochita zake chakumanzere kudzera kumbuyo kwa msana wake (chifukwa chomunyoza),
Share