Surah Abasa ( He frowned ) - Aya 23

Surah Abasa ( He frowned ) - Chewa - Aya 23 Aya count 42

كَلَّا لَمَّا يَقْضِ مَآ أَمَرَهُۥ ﴿٢٣﴾
Ayi ndithu (munthu) sanakwaniritsebe zimene adamulamula Mbuye wake (Allah chingakhale wakhala nthawi yaitali pa dziko lapansi).
Share