Surah Abasa ( He frowned ) - Aya 2

Surah Abasa ( He frowned ) - Chewa - Aya 2 Aya count 42

أَن جَآءَهُ ٱلْأَعْمَىٰ ﴿٢﴾
Chifukwa chakuti adamdzera wakhungu (kudzamfunsa zokhudzana ndi chipembedzo chake pamene iye adali kuyankhula ndi atsogoleri Achiquraishi).
Share