Surah Al-Muddaththir ( The One Enveloped ) - Aya 37

Surah Al-Muddaththir ( The One Enveloped ) - Chewa - Aya 37 Aya count 56

لِمَن شَآءَ مِنكُمْ أَن يَتَقَدَّمَ أَوْ يَتَأَخَّرَ ﴿٣٧﴾
Kwa yemwe wafuna mwa inu kutsogola (pochita zabwino zokamthandiza tsiku louka kwa akufa) kapena kutsalira (ndi za m’dziko).
Share