Surah Al-Ma'arij (The Ways of Ascent ) - Aya 43

Surah Al-Ma'arij (The Ways of Ascent ) - Chewa - Aya 43 Aya count 44

يَوْمَ يَخْرُجُونَ مِنَ ٱلْأَجْدَاثِ سِرَاعًۭا كَأَنَّهُمْ إِلَىٰ نُصُبٍۢ يُوفِضُونَ ﴿٤٣﴾
Tsiku limene adzatuluke m’manda uku akuthamanga (kudza kwa woitana) ngati kuti akuthamangira kumafano awo (amene adali kuwapembedza).
Share