Surah Al-Waqi'ah ( The Event ) - Aya 73

Surah Al-Waqi'ah ( The Event ) - Chewa - Aya 73 Aya count 96

نَحْنُ جَعَلْنَٰهَا تَذْكِرَةًۭ وَمَتَٰعًۭا لِّلْمُقْوِينَ ﴿٧٣﴾
Ife taupanga kuti ukhale chikumbutso (cha Moto watsiku lachimaliziro akauona), ndikuti ukhale chothandiza kwa anthu apaulendo (amene akuyenda m’chipululu).
Share