Surah Al-Waqi'ah ( The Event ) - Aya 59

Surah Al-Waqi'ah ( The Event ) - Chewa - Aya 59 Aya count 96

ءَأَنتُمْ تَخْلُقُونَهُۥٓ أَمْ نَحْنُ ٱلْخَٰلِقُونَ ﴿٥٩﴾
Kodi inu ndiamene mumawalenga (madziwo ndi kumayang’anira mkusinthasintha kwake kuti akhale cholengedwa) kapena Ife ndiamene timawalenga?
Share