Surah Adh-Dhariyat ( The Wind that Scatter ) - Aya 39

Surah Adh-Dhariyat ( The Wind that Scatter ) - Chewa - Aya 39 Aya count 60

فَتَوَلَّىٰ بِرُكْنِهِۦ وَقَالَ سَٰحِرٌ أَوْ مَجْنُونٌۭ ﴿٣٩﴾
Koma Farawo adanyoza (kukhulupirira Mûsa) chifukwa chotama nyonga zake, ndipo adati: “Uyu ndi wamatsenga kapena wamisala.”
Share