Surah Adh-Dhariyat ( The Wind that Scatter ) - Aya 28

Surah Adh-Dhariyat ( The Wind that Scatter ) - Chewa - Aya 28 Aya count 60

فَأَوْجَسَ مِنْهُمْ خِيفَةًۭ ۖ قَالُوا۟ لَا تَخَفْ ۖ وَبَشَّرُوهُ بِغُلَٰمٍ عَلِيمٍۢ ﴿٢٨﴾
Mumtima mwake adadzazidwa mantha ndi iwo. Iwo adati: “Usaope,” ndipo adamuuza nkhani yabwino ya kubala mwana wodziwa.
Share