Surah Az-Zumar ( The Groups ) - Aya 1

Surah Az-Zumar ( The Groups ) - Chewa - Aya 1 Aya count 75

تَنزِيلُ ٱلْكِتَٰبِ مِنَ ٱللَّهِ ٱلْعَزِيزِ ٱلْحَكِيمِ ﴿١﴾
Kuvumbulutsidwa kwa Buku ili kwachokera kwa Allah, Mwini mphamvu zoposa; Mwini nzeru zakuya.
Share