Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Aya 51

Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Chewa - Aya 51 Aya count 182

قَالَ قَآئِلٌۭ مِّنْهُمْ إِنِّى كَانَ لِى قَرِينٌۭ ﴿٥١﴾
Adzanena wonena mmodzi wa iwo: “Ine ndidali ndi mnzanga (wopembedza mafano amene amatsutsana nane za chipembedzo ndi zophunzitsa za Qur’an yolemekezeka).”
Share