Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Aya 28

Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Chewa - Aya 28 Aya count 182

قَالُوٓا۟ إِنَّكُمْ كُنتُمْ تَأْتُونَنَا عَنِ ٱلْيَمِينِ ﴿٢٨﴾
Ndipo (ofooka) adzanena (kwa odzikweza): “Inu mumatidzera kumbali komwe timakuganizira kuti nkwabwino (ndi kutichotsako kunka nafe ku njira yopotoka).
Share