Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Aya 22

Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Chewa - Aya 22 Aya count 182

۞ ٱحْشُرُوا۟ ٱلَّذِينَ ظَلَمُوا۟ وَأَزْوَٰجَهُمْ وَمَا كَانُوا۟ يَعْبُدُونَ ﴿٢٢﴾
(Kudzanenedwa kwa angelo): “Asonkhanitseni amene adali osalungama pamodzi ndi akazi awo (okana Allah) ndi milungu yawo imene amaipembedza,”
Share