Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Aya 112

Surah As-Saaffat ( Those Ranges in Ranks ) - Chewa - Aya 112 Aya count 182

وَبَشَّرْنَٰهُ بِإِسْحَٰقَ نَبِيًّۭا مِّنَ ٱلصَّٰلِحِينَ ﴿١١٢﴾
Ndiponso tidamuuza nkhani yabwino (yoti akhala ndi mwana wotchedwa) Isihaqa; mneneri; wam’gulu la olungama.
Share