Surah Ya-seen - Aya 3

Surah Ya-seen - Chewa - Aya 3 Aya count 83

إِنَّكَ لَمِنَ ٱلْمُرْسَلِينَ ﴿٣﴾
Ndithu iwe (Muhammad {s.a.w}) ndimmodzi wa atumiki (amene Allah adawatuma kwa anthu kuti akawasonyeze chiongoko).
Share