Surah Fatir ( The Orignator ) - Aya 44

Surah Fatir ( The Orignator ) - Chewa - Aya 44 Aya count 45

أَوَلَمْ يَسِيرُوا۟ فِى ٱلْأَرْضِ فَيَنظُرُوا۟ كَيْفَ كَانَ عَٰقِبَةُ ٱلَّذِينَ مِن قَبْلِهِمْ وَكَانُوٓا۟ أَشَدَّ مِنْهُمْ قُوَّةًۭ ۚ وَمَا كَانَ ٱللَّهُ لِيُعْجِزَهُۥ مِن شَىْءٍۢ فِى ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَلَا فِى ٱلْأَرْضِ ۚ إِنَّهُۥ كَانَ عَلِيمًۭا قَدِيرًۭا ﴿٤٤﴾
Kodi sadayende pa dziko nkuona momwe adalili mathero a omwe adali patsogolo pawo? Ndipo adali anyonga kwambiri kuposa iwo? Ndipo palibe chinthu chonkanika Allah kumwamba ndi pansi. Ndithudi Iye Ngodziwa kwabasi Wokhoza.
Share