Surah Al-Ahzab ( The Combined Forces ) - Aya 46

Surah Al-Ahzab ( The Combined Forces ) - Chewa - Aya 46 Aya count 73

وَدَاعِيًا إِلَى ٱللَّهِ بِإِذْنِهِۦ وَسِرَاجًۭا مُّنِيرًۭا ﴿٤٦﴾
Ndi kuti ukhale woitanira (anthu) kwa Allah kupyolera m’chifuniro Chake. Ndi (kutinso ukhale) nyali younikira (anthu).
Share