Surah Al-Imran ( The Famiy of Imran ) - Aya 138

Surah Al-Imran ( The Famiy of Imran ) - Chewa - Aya 138 Aya count 200

هَٰذَا بَيَانٌۭ لِّلنَّاسِ وَهُدًۭى وَمَوْعِظَةٌۭ لِّلْمُتَّقِينَ ﴿١٣٨﴾
Uku ndi kulengeza poyera kwa anthu (onse); komanso chiongoko ndi ulaliki kwa (anthu) oopa Allah!
Share