Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Aya 83

Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Chewa - Aya 83 Aya count 227

رَبِّ هَبْ لِى حُكْمًۭا وَأَلْحِقْنِى بِٱلصَّٰلِحِينَ ﴿٨٣﴾
“E Mbuye wanga! Ndipatseni nzeru zoweruzira (zinthu), ndikundilumikiza ndi anthu abwino;”
Share