Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Aya 70

Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Chewa - Aya 70 Aya count 227

إِذْ قَالَ لِأَبِيهِ وَقَوْمِهِۦ مَا تَعْبُدُونَ ﴿٧٠﴾
Pamene adafunsa bambo wake ndi anthu ake (kuti); “Kodi mukupembedza chiyani?”
Share