Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Aya 27

Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Chewa - Aya 27 Aya count 227

قَالَ إِنَّ رَسُولَكُمُ ٱلَّذِىٓ أُرْسِلَ إِلَيْكُمْ لَمَجْنُونٌۭ ﴿٢٧﴾
(Farawo) adati (kwa anthu ake pofuna kuwakwiitsa): “Ndithu Mtumiki wanu amene watumidwa kwa inu, ngwamisala.”
Share