Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Aya 188

Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Chewa - Aya 188 Aya count 227

قَالَ رَبِّىٓ أَعْلَمُ بِمَا تَعْمَلُونَ ﴿١٨٨﴾
(Shuaib) adati: “Mbuye wanga Ngodziwa kwambiri zimene mukuchita. (Akadzaona kuti inu ngoyenera kulangidwa ndizidutswa za thambo, adzakulangani).”
Share