Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Aya 111

Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Chewa - Aya 111 Aya count 227

۞ قَالُوٓا۟ أَنُؤْمِنُ لَكَ وَٱتَّبَعَكَ ٱلْأَرْذَلُونَ ﴿١١١﴾
(Iwo) adati: “Nchotani kuti tikukhulupirire iwe chikhalirecho anthu wamba ndi amene akukutsatira?”
Share