Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Aya 10

Surah Ash-Shuara ( The Poets ) - Chewa - Aya 10 Aya count 227

وَإِذْ نَادَىٰ رَبُّكَ مُوسَىٰٓ أَنِ ٱئْتِ ٱلْقَوْمَ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴿١٠﴾
Ndipo (akumbutse) pamene Mbuye wako adaitana (m’neneri) Mûsa; adamuuza: “Pita kwa anthu ochita zoipa.”
Share