Surah Al-Furqan (The Criterion ) - Aya 56

Surah Al-Furqan (The Criterion ) - Chewa - Aya 56 Aya count 77

وَمَآ أَرْسَلْنَٰكَ إِلَّا مُبَشِّرًۭا وَنَذِيرًۭا ﴿٥٦﴾
Ndipo Ife sitidakutume koma kuti ukhale wouza nkhani zabwino (okhulupirira); ndi wochenjeza (osakhulupirira).
Share