Surah Al-Anbiya ( The Prophets ) - Aya 95

Surah Al-Anbiya ( The Prophets ) - Chewa - Aya 95 Aya count 112

وَحَرَٰمٌ عَلَىٰ قَرْيَةٍ أَهْلَكْنَٰهَآ أَنَّهُمْ لَا يَرْجِعُونَ ﴿٩٥﴾
Ndipo nkosatheka kwa eni mudzi umene tidauononga chifukwa cha machimo awo kuti asabwelere kwa Ife; (koma ndithu abwerera).
Share