Surah Al-Anbiya ( The Prophets ) - Aya 64

Surah Al-Anbiya ( The Prophets ) - Chewa - Aya 64 Aya count 112

فَرَجَعُوٓا۟ إِلَىٰٓ أَنفُسِهِمْ فَقَالُوٓا۟ إِنَّكُمْ أَنتُمُ ٱلظَّٰلِمُونَ ﴿٦٤﴾
Ndipo adadzitembenukira okha ndikunena kuti: “Ndithu inu ndinu oipa.”
Share