Surah Al-Anbiya ( The Prophets ) - Aya 59

Surah Al-Anbiya ( The Prophets ) - Chewa - Aya 59 Aya count 112

قَالُوا۟ مَن فَعَلَ هَٰذَا بِـَٔالِهَتِنَآ إِنَّهُۥ لَمِنَ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴿٥٩﴾
(Iwo parnene adafika kumafano awo) adati: “Ndani wachita ichi pa milungu yathu? Ndithu iye ndi m’modzi wa ochita zoipa.”
Share