Surah Al-Hijr ( The Rocky Tract ) - Aya 2

Surah Al-Hijr ( The Rocky Tract ) - Chewa - Aya 2 Aya count 99

رُّبَمَا يَوَدُّ ٱلَّذِينَ كَفَرُوا۟ لَوْ كَانُوا۟ مُسْلِمِينَ ﴿٢﴾
Nthawi zambiri omwe sadakhulupirire (pamene adzakhala m’Moto) adzalakalaka kuti akadakhala okhulupirira (pamoyo wa pa dziko lapansi).
Share