Surah Ibrahim ( Abraham ) - Aya 16

Surah Ibrahim ( Abraham ) - Chewa - Aya 16 Aya count 52

مِّن وَرَآئِهِۦ جَهَنَّمُ وَيُسْقَىٰ مِن مَّآءٍۢ صَدِيدٍۢ ﴿١٦﴾
(Yemwe) kutsogolo kwake Jahannam ikumdikira, ndipo (kumeneko) adzamumwetsa madzi amafinya (otuluka m’matupi a anthu a ku Moto).
Share