Surah Al-Kauther ( A River in Paradise) - Aya 2

Surah Al-Kauther ( A River in Paradise) - Chewa - Aya 2 Aya count 3

فَصَلِّ لِرَبِّكَ وَٱنْحَرْ ﴿٢﴾
(Pakuti ndakupatsa zimenezo), pitiriza kupembedza Mbuye wako (moyera mtima) ndipo ipha nsembe yako (chifukwa chakuthokoza Allah pa zimene wakupatsa, monga ulemelero ndikukusankhira zabwino zambiri).[491]
Share