Surah Al-Kauther ( A River in Paradise)

Surah Al-Kauther ( A River in Paradise) - Chewa Aya count 3

Ndithu takupatsa zabwino zambiri (zina mwa izo ndi mtsinje wotchedwa Kauthar).[490]
(Pakuti ndakupatsa zimenezo), pitiriza kupembedza Mbuye wako (moyera mtima) ndipo ipha nsembe yako (chifukwa chakuthokoza Allah pa zimene wakupatsa, monga ulemelero ndikukusankhira zabwino zambiri).[491]
Ndithu mdani wako ndiye ali wopanda mwawi. [492]
Share