Surah Al-Ma'un ( Small Kindnesses ) - Aya 7

Surah Al-Ma'un ( Small Kindnesses ) - Chewa - Aya 7 Aya count 7

وَيَمْنَعُونَ ٱلْمَاعُونَ ﴿٧﴾
Ndipo amamana ziwiya (zawo posabwereka anzawo zinthu zofunika pa moyo wa aliyense monga nkhwangwa, mpeni, mtondo ndi zina zotere).
Share