Surah Al-Ma'un ( Small Kindnesses ) - Aya 6

Surah Al-Ma'un ( Small Kindnesses ) - Chewa - Aya 6 Aya count 7

ٱلَّذِينَ هُمْ يُرَآءُونَ ﴿٦﴾
Amenenso (akamachita mapemphero awo) amadzionetsera (kwa anthu mwachipha maso kuti apeze ulemelero ndi kutamandidwa mmitima mwa anthu).[489]
Share