Surah Quraish - Aya 4

Surah Quraish - Chewa - Aya 4 Aya count 4

ٱلَّذِىٓ أَطْعَمَهُم مِّن جُوعٍۢ وَءَامَنَهُم مِّنْ خَوْفٍۭ ﴿٤﴾
Yemwe amawadyetsa (nthawi imene Arabu anzawo) ali m’njala, ndipo amawapatsa chitetezo (pomwe anzawo) ali ndi mantha.
Share