Surah Yunus ( Jonah ) - Aya 40

Surah Yunus ( Jonah ) - Chewa - Aya 40 Aya count 109

وَمِنْهُم مَّن يُؤْمِنُ بِهِۦ وَمِنْهُم مَّن لَّا يُؤْمِنُ بِهِۦ ۚ وَرَبُّكَ أَعْلَمُ بِٱلْمُفْسِدِينَ ﴿٤٠﴾
Ndipo mwa iwo pali ena omwe akuikhulupirira (Qur’an), ndipo ena mwa iwo sakuikhulupirira. Ndipo Mbuye wako akuwadziwa bwino oononga.
Share