Surah Az-Zalzalah ( The Earthquake ) - Aya 6

Surah Az-Zalzalah ( The Earthquake ) - Chewa - Aya 6 Aya count 8

يَوْمَئِذٍۢ يَصْدُرُ ٱلنَّاسُ أَشْتَاتًۭا لِّيُرَوْا۟ أَعْمَٰلَهُمْ ﴿٦﴾
Tsiku limenelo anthu adzachoka (m’manda) ali m’magulu obalalika kuti akasonyezedwe ntchito zawo (ndikudziwa chiwerengero chawo chimene chili kwa Allah).
Share