Surah Az-Zalzalah ( The Earthquake ) - Aya 3

Surah Az-Zalzalah ( The Earthquake ) - Chewa - Aya 3 Aya count 8

وَقَالَ ٱلْإِنسَٰنُ مَا لَهَا ﴿٣﴾
Ndipo munthu adzanena (mwa mantha, ndikudabwa nthawi imeneyo). Ha! Yatani nthaka, (kodi Qiyâma yafika)?
Share