Surah Ash-Shams ( The Sun ) - Aya 15

Surah Ash-Shams ( The Sun ) - Chewa - Aya 15 Aya count 15

وَلَا يَخَافُ عُقْبَٰهَا ﴿١٥﴾
Iye saopa zotsatira za chilangochi (chifukwa amenewa ndi malipiro a chilungamo pa zomwe adachita).
Share