Surah Al-Muzzammil (The One wrapped in Garments) - Aya 7

Surah Al-Muzzammil (The One wrapped in Garments) - Chewa - Aya 7 Aya count 20

إِنَّ لَكَ فِى ٱلنَّهَارِ سَبْحًۭا طَوِيلًۭا ﴿٧﴾
Ndithu masana uli ndi zochitachita zambiri; (umatanganidwa ndi ntchito yauthenga; dzipatse danga usiku polimbika kupemphera).
Share