Surah Al-Muzzammil (The One wrapped in Garments) - Aya 14

Surah Al-Muzzammil (The One wrapped in Garments) - Chewa - Aya 14 Aya count 20

يَوْمَ تَرْجُفُ ٱلْأَرْضُ وَٱلْجِبَالُ وَكَانَتِ ٱلْجِبَالُ كَثِيبًۭا مَّهِيلًا ﴿١٤﴾
Tsiku limene nthaka ndi mapiri zidzagwedezeka; (kugwedezeka kwa mphamvu kotero kuti) mapiri adzakhala ngati mulu wa mchenga woyoyoka.
Share