Surah Al-Jinn ( The Jinn ) - Aya 7

Surah Al-Jinn ( The Jinn ) - Chewa - Aya 7 Aya count 28

وَأَنَّهُمْ ظَنُّوا۟ كَمَا ظَنَنتُمْ أَن لَّن يَبْعَثَ ٱللَّهُ أَحَدًۭا ﴿٧﴾
Ndipo ndithu iwo amaganiza monga momwe mumaganizira inu kuti Allah sadzaukitsa aliyense.
Share