Surah Al-Jinn ( The Jinn ) - Aya 3

Surah Al-Jinn ( The Jinn ) - Chewa - Aya 3 Aya count 28

وَأَنَّهُۥ تَعَٰلَىٰ جَدُّ رَبِّنَا مَا ٱتَّخَذَ صَٰحِبَةًۭ وَلَا وَلَدًۭا ﴿٣﴾
Ndipo ndithu ukulu ndi ulemelero wa Mbuye wathu watukuka; sadadzipangire mkazi kapena mwana.
Share