Surah Al-Qalam ( The Pen ) - Aya 18

Surah Al-Qalam ( The Pen ) - Chewa - Aya 18 Aya count 52

وَلَا يَسْتَثْنُونَ ﴿١٨﴾
Ndipo sadapatule (ngakhale wosauka ndi m’modzi yemwe ponena kuti uje timpatse, uje tisampatse, kapena sadanene kuti: “Ngati Allah afuna).”
Share